Psalms 119:104 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimakhala ndi nzeru za kumvetsa chifukwa cha malamulo anu. Nchifukwa chake ndimadana ndi njira iliyonse yonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Malangizo anu andizindikiritsa; chifukwa chake ndidana nao mayendedwe onse achinyengo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimapeza nzeru zodziwira zinthu kuchokera mʼmalangizo anu; kotero ndimadana ndi njira iliyonse yoyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Malangizo anu andizindikiritsa; Cifukwa cace ndidana nao mayendedwe onse acinyengo,