Psalms 119:105 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mau anu ndiye nyale ya mapazi anga, ndipo amaunikira njira yanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga, ndi kuunika kwa panjira panga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu anu ndi nyale ya kumapazi kwanga ndi kuwunika kwa pa njira yanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga, Ndi kuunika kwa panjira panga,