Psalms 119:106 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndalumbirira, ndipo ndatsimikiza kuti ndidzamvera malangizo anu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinalumbira, ndipo ndinatsimikiza mtima, kuti ndidzasamalira maweruzo anu olungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndalumbira ndipo ndatsimikiza, kuti ndidzatsatira malamulo anu olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinalumbira, ndipo ndinatsimikiza mtima, Kuti ndidzasamalira maweruzo anu olungama.