Psalms 119:107 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndazunzika koopsa, Chauta, patseni moyo, molingana ndi mau anu aja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndazunzika kwambiri: Ndipatseni moyo, Yehova, monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndazunzika kwambiri; Inu Yehova, sungani moyo wanga molingana ndi mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndazunzika kwambiri: Ndipatseni moyo, Yehova, monga mwa mau anu.