Psalms 119:109 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Moyo wanga uli m'zoopsa nthaŵi zonse, komabe sindiiŵala malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga ukhala m'dzanja langa chikhalire; koma sindiiwala chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale moyo wanga umakhala mʼzoopsa nthawi ndi nthawi, sindidzayiwala malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga ukhala m'dzanja langa cikhalire; Koma sindiiwala cilamulo canu.