Psalms 119:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndasunga mau anu mumtima mwanga, kuti ndisakuchimwireni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinawabisa mau anu mumtima mwanga, kuti ndisalakwire Inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndasunga mawu anu mu mtima mwanga kuti ndisakuchimwireni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinawabisa mau anu mumtima mwanga, Kuti ndisalakwire Inu.