Psalms 119:111 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu ndiye madalitso anga mpaka muyaya, zoonadi, ndiwo amene amasangalatsa mtima wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinalandira mboni zanu zikhale cholandira chosatha; pakuti ndizo zokondweretsa mtima wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Umboni wanu ndiye cholowa changa kwamuyaya; Iwo ndiye chimwemwe cha mtima wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinalandira mboni zanu zikhale colandira cosatha; Pakuti ndizo zokondweretsa mtima wanga.