Psalms 119:112 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wanga muuphunzitse kuti uzikonda malamulo anu nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinalingitsa mtima wanga uchite malemba anu, kosatha, kufikira chimaliziro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wanga wakhazikika pa kusunga zophunzitsa zanu mpaka kumapeto kwenikweni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinalingitsa mtima wanga ucite malemba anu, Kosatha, kufikira cimatiziro.