Psalms 119:113 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimadana nawo anthu apaŵiripaŵiri, koma ndimakonda mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidana nao a mitima iwiri; koma ndikonda chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimadana ndi anthu apawiripawiri, koma ndimakonda malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidana nao a mitima iwiri; Koma ndikonda cilamulo canu.