Psalms 119:116 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chirikizeni molingana ndi malonjezo anu aja, kuti ndizikhala ndi moyo, ndipo anthu asandichititse manyazi, chifukwa ndine wokhulupirika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mundichirikize monga mwa mau anu, kuti ndikhale ndi moyo; ndipo ndisachite manyazi pa chiyembekezo changa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mundichirikize molingana ndi lonjezo lanu, ndipo ndidzakhala ndi moyo; musalole kuti chiyembekezo changa chipite pachabe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mundicirikize monga mwa mau anu, kuti ndikhale ndi moyo; Ndipo ndisacite manyazi pa ciyembekezo canga.