Psalms 119:120 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Thupi langa limanjenjemera chifukwa chokuwopani, ndimachita mantha ndi kuweruza kwanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Thupi langa linjenjemera ndi kuopa Inu; ndipo ndichita mantha nao maweruzo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Thupi langa limanjenjemera chifukwa cha kuopa Inu; ndimachita mantha ndi malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Thupi langa linjenjemera ndi kuopa Inu; Ndipo ndicita mantha nao maweruzo anu.