Psalms 119:121 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndachita zimene zili zolungama ndi zabwino. Musandisiye m'manja mwa ondizunza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinachita chiweruzo ndi chilungamo; musandisiyira akundisautsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndachita zolungama ndi zabwino; musandisiye mʼmanja mwa ondizunza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinacita ciweruzo ndi cilungamo; Musandisiyira akundisautsa.