Psalms 119:123 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maso anga atopa chifukwa cha kuyembekeza chipulumutso chanu, chifukwa cha kudikira kuti malonjezo anu olungama aja achitikedi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso anga anatha mphamvu pofuna chipulumutso chanu, ndi mau a chilungamo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maso anga alefuka, kufunafuna chipulumutso chanu, kufunafuna lonjezo lanu lolungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso anga anatha mphamvu pafuna cipulumutso canu, Ndi mau a cilungamo canu.