Psalms 119:124 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komereni mtima mtumiki wanune, chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika, ndipo mundiphunzitse malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muchitire mtumiki wanu monga mwa chifundo chanu, ndipo ndiphunzitseni malemba anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Muchite naye mtumiki wanu molingana ndi chikondi chanu chosasinthika, ndipo mundiphunzitse malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mucitire mtumiki wanu monga mwa cifundo canu, Ndipo ndiphunzitseni malemba anu,