Psalms 119:126 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yakwana nthaŵi yakuti Inu Chauta muchitepo kanthu, popeza kuti anthu aphwanya malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yafika nyengo yakuti Yehova achite kanthu; pakuti anaswa chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova, ndi nthawi yoti muchitepo kanthu; malamulo anu akuswedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yafika nyengo yakuti Yehova acite kanthu; Pakuti anaswa cilamulo canu.