Psalms 119:128 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu onse amalungamitsa mayendedwe anga. Ndimadana ndi njira iliyonse yonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndiponso chifukwa choti ndimaona kuti malangizo anu onse ndi wowongoka, ndimadana ndi njira iliyonse yoyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; Koma ndidana nazo njira zonse zonyenga.