Psalms 119:129 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu ndi abwino, nchifukwa chake ndimaŵatsata ndi mtima wanga wonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mboni zanu nzodabwitsa; chifukwa chake moyo wanga uzisunga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maumboni anu ndi odabwitsa nʼchifukwa chake ndimawamvera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mboni zanu nzodabwiza; Cifukwa cace moyo wanga uzisunga,