Psalms 119:132 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yang'aneni, ndipo mundikomere mtima monga m'mene mumachitira ndi anthu okukondani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munditembenukire, ndi kundichitira chifundo, monga mumatero nao akukonda dzina lanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tembenukirani kwa ine ndipo mundichitire chifundo, monga mumachitira nthawi zonse kwa iwo amene amakonda dzina lanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munditembenukire, ndi kundicitira cifundo, Monga mumatero nao akukonda dzina lanu.