Psalms 119:136 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maso anga akudza misozi yambiri ngati mitsinje, chifukwa anthu satsata malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso anga atsitsa mitsinje ya madzi, popeza sasamalira chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mitsinje ya misozi ikuyenda kuchoka mʼmaso mwanga, chifukwa anthu sakumvera malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso anga atsitsa mitsinje ya madzi, Popeza sasamalira cilamulo canu.