Psalms 119:139 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Changu changa chikuyaka ngati moto mumtima mwanga, chifukwa adani anga amaiŵala mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndikusautsidwa kwambiri mʼkati mwanga chifukwa adani anu amanyalanyaza mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cangu canga cinandithera, Popeza akundisautsa anaiwala mau anu.