Psalms 119:144 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu ndi olungama mpaka muyaya, patseni nzeru zomvetsa kuti ndizikhala ndi moyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mboni zanu ndizo zolungama kosatha; mundizindikiritse izi, ndipo ndidzakhala ndi moyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Umboni wanu ndi wabwino nthawi zonse; patseni nzeru zomvetsa zinthu kuti ine ndikhale ndi moyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mboni zanu ndizo zolungama kosatha; Mundizindikiritse izi, ndipo ndidzakhala ndi moyo.