Psalms 119:145 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikulira kwa Inu ndi mtima wanga wonse, mundiyankhe, Inu Chauta. Ndidzatsata malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinaitana ndi mtima wanga wonse; mundiyankhe, Yehova; ndidzasunga malemba anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimayitana ndi mtima wanga wonse; ndiyankheni Inu Yehova, ndipo ndidzamvera zophunzitsa zanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinaitana ndi mtima wanga wonse; mundiyankhe, Yehova; Ndidzasunga malemba anu.