Psalms 119:149 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Imvani liwu langa chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika. Inu Chauta, sungani moyo wanga chifukwa cha chilungamo chanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Imvani liu langa monga mwa chifundo chanu; mundipatse moyo monga mwa kuweruza kwanu, Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Imvani mawu anga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; Yehova sungani moyo wanga, molingana ndi malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Imvani liu langa monga mwa cifundo canu; Mundipatse moyo monga mwa kuweruza kwanu, Yehova.