Psalms 119:150 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu ankhanza ondizunza akuyandikira. Iwo ali kutali ndi malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Otsata zachiwembu andiyandikira; akhala kutali ndi chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amene amakonza njira zoyipa andiyandikira, koma ali kutali ndi malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Otsata zaciwembu andiyandikira; Akhala kutali ndi cilamulo canu.