Psalms 119:158 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimanyansidwa ndikamayang'ana anthu osakhulupirika, chifukwa satsata malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinapenya ochita monyenga, ndipo ndinanyansidwa nao; popeza sasamalira mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimawayangʼana monyansidwa anthu opanda chikhulupiriro, popeza samvera mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinapenya ocita monyenga, ndipo ndinanyansidwa nao; Popeza sasamalira mau anu.