Psalms 119:159 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Onani m'mene ndimakondera malamulo anu, sungani moyo wanga chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Penyani kuti ndikonda malangizo anu; mundipatse moyo, Yehova, monga mwa chifundo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Onani momwe ndimakondera malangizo anu; sungani moyo wanga, Inu Yehova, molingana ndi chikondi chanu chosanthika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Penyani kuti ndikonda malangizo anu; Mundipatse moyo, Yehova, monga mwa cifundo canu.