Psalms 119:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakondwera ndi malamulo anu, ndipo mau anu sindidzaŵaiŵala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimakondwera ndi malamulo anu; sindidzayiwala konse mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; Sindidzaiwala mau anu,