Psalms 119:162 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimakondwa ndi mau anu monga munthu amene wapeza chuma chambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikondwera nao mau anu, ngati munthu wakupeza zofunkha zambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndimakondwa ndi lonjezo lanu, ngati munthu amene wapeza chuma chambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikondwera nao mau anu, Ngati munthu wakupeza zofunkha zambiri.