Psalms 119:163 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimadana ndi anthu abodza, zoonadi, ndimanyansidwa nawo, koma ndimakonda malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidana nalo bodza ndi kunyansidwa nalo; koma ndikonda chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimadana ndi chinyengo, kwambiri ndimanyansidwa nacho, koma ndimakonda malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidana nalo bodza ndi kunyansidwa nalo; Koma ndikonda cilamulo canu.