Psalms 119:164 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimakutamandani kasanunkaŵiri pa tsiku, chifukwa cha malangizo anu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikulemekezani kasanu ndi kawiri, tsiku limodzi, chifukwa cha maweruzo anu alungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimakutamandani kasanu ndi kawiri pa tsiku pakuti malamulo anu ndi olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikulemekezani kasanu ndi kawiri, tsiku limodzi, Cifukwa ca maweruzo anu alungama.