Psalms 119:167 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mzimu wanga umatsata malamulo anu, pakuti ndimaŵakonda ndi mtima wanga wonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga unasamalira mboni zanu; ndipo ndizikonda kwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimamvera umboni wanu pakuti ndimawukonda kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga unasamalira mboni zanu; Ndipo ndizikonda kwambiri.