Psalms 119:168 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimatsata malamulo anu ndi malangizo anu, pakuti makhalidwe anga onse mukuŵaona.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinasamalira malangizo anu ndi mboni zanu; popeza njira zanga zonse zili pamaso panu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimamvera malangizo anu ndi umboni wanu, pakuti njira zanga zonse ndi zodziwika pamaso panu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinasamalira malangizo anu ndi mboni zanu; Popeza njira zanga zonse ziri pamaso panu,