Psalms 119:169 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kulira kwanga kumveke kwa Inu, Chauta. Mundipatse nzeru zomvetsa potsata mau anu aja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kufuula kwanga kuyandikire pamaso panu, Yehova; mundizindikiritse monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kulira kwanga kufike pamaso panu Yehova; patseni nzeru zomvetsa zinthu molingana ndi mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kupfuula kwanga kuyandikire pamaso pano, Yehova; Mundizindikiritse monga mwa mau anu.