Psalms 119:170 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kupempha kwanga kumveke kwa Inu. Mundipulumutse potsata malonjezo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kupemba kwanga kudze pamaso panu; mundilanditse monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kupempha kwanga kufike pamaso panu; pulumutseni molingana ndi lonjezo lanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kupemba kwanga kudze pamaso panu; Mundilanditse monga mwa mau anu.