Psalms 119:172 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzaimba nyimbo zoyamikira mau anu, chifukwa malamulo anu onse ndi olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lilime langa liimbire mau anu; pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Lilime langa liyimbe mawu anu, popeza malamulo anu onse ndi olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lilime langa liyimbire mau anu; Pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama.