Psalms 119:176 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndasokera ngati nkhosa yoloŵerera, koma mundifunefune ine mtumiki wanu, pakuti sindiiŵala malamulo anu. Nyimbo yoimba pokwera ku Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinasochera ngati nkhosa yotayika; funani mtumiki wanu; pakuti sindiiwala malamulo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndasochera ngati nkhosa yotayika, funafunani mtumiki wanu, pakuti sindinayiwale malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinasocera ngati nkhosa yotayika; funani mtumiki wanu; Pakuti sindiiwala malamulo anu.