Psalms 119:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngodala amene amasunga malamulo a Chauta, amene amafunafuna Chauta ndi mtima wao wonse,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Odala ndi amene amasunga malamulo ake, amene amafunafuna Iyeyo ndi mtima wawo wonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odala iwo akusunga mboni zace, Akumfuna ndi mtima wonse;