Psalms 119:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wanga wafooka chifukwa cholakalaka malangizo anu nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wanga wasweka ndi kukhumba maweruzo anu nyengo zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moyo wanga wafowoka polakalaka malamulo anu nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wanga wasweka ndi kukhumba Maweruzo anu nyengo zonse.