Psalms 119:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndangoti thapsa m'fumbi. Bwezereni moyo monga momwe mudalonjezera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moyo wanga wakangamira fumbi; tsitsimutseni molingana ndi mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga umamatika ndi pfumbi; Mundipatse moyo monga mwa mau anu.