Psalms 119:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndafookeratu ndi chisoni. Limbitseni monga momwe mudalonjezera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga wasungunuka ndi chisoni: Mundilimbitse monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moyo wanga wafowoka ndi chisoni; limbikitseni monga mwa mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga wasungunuka ndi cisoni: Mundilimbitse monga mwa mau anu.