Psalms 119:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndasankhula njira yoti ndizikhala wokhulupirika, ndaika malangizo anu mumtima mwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinasankha njira yokhulupirika; ndinaika maweruzo anu pamaso panga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndasankha njira ya choonadi; ndayika malamulo anu pa mtima panga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinasankha njira yokhulupirika; Ndinaika maweruzo anu pamaso, panga,