Psalms 119:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzatsata mokondwa njira ya malamulo anu, mukandiwonjezera nzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzathamangira njira ya malamulo anu, mutakulitsa mtima wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimathamanga mʼnjira ya malamulo anu, pakuti Inu mwamasula mtima wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzathamangira njira ya malamulo anu, Mutakulitsa mtima wanga.