Psalms 119:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta, phunzitseni njira zosungira malamulo anu, ndipo ndidzazitsata mpaka kumathero.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mundiphunzitse, Yehova, njira ya malemba anu; ndidzaisunga kufikira kutha kwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova, phunzitseni kutsatira zophunzitsa zanu; ndipo ndidzazisunga mpaka kumapeto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mundiphunzitse, Yehova, njira ya malemba anu; Ndidzaisunga kufikira kutha kwace.