Psalms 119:34 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patseni nzeru kuti ndizisunga malamulo anu, ndiziŵatsata ndi mtima wanga wonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mundizindikiritse, ndipo ndidzasunga malamulo anu; ndidzawasamalira ndi mtima wanga wonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mundipatse mtima womvetsa zinthu ndipo ndidzasunga malamulo anu ndi kuwamvera ndi mtima wanga wonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mundizindikiritse, ndipo ndidzasunga malamulo anu; Ndidzawasamalira ndi mtima wanga wonse.