Psalms 119:36 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muphunzitse mtima wanga kuti uzikonda malamulo anu, osati chuma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lingitsani mtima wanga kumboni zanu, si ku chisiriro ai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tembenuzani mtima wanga kuti uzikonda malamulo anu, osati chuma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lingitsani mtima wanga ku mboni zanu, Si ku cisiriro ai.