Psalms 119:37 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Letsani maso anga kuti asamayang'ane zachabe, mundipatse moyo monga momwe mudalonjezera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muchititse mlubza maso anga ndisapenye zachabe, mundipatse moyo mu njira yanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tembenuzani maso anga kuchoka ku zinthu zachabechabe; sungani moyo wanga monga mwa mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mucititse mlubza maso anga ndisapenye zacabe, Mundipatse moyo mu njira yanu.