Psalms 119:38 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munditsimikizire ine mtumiki wanu chipangano chanu, chimene mumachita ndi anthu okuwopani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Limbitsirani mtumiki wanu mau anu, ndiye wodzipereka kukuopani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kwaniritsani lonjezo lanu kwa mtumiki wanu, kuti Inu muopedwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Limbitsirani mtumiki wanu mau anu, Ndiye wodzipereka kukuopani.