Psalms 119:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Onani ndikulakalaka kutsata malamulo anu. Mundipatse moyo chifukwa ndinu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ndinalira malangizo anu; mundipatse moyo mwa chilungamo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Taonani, ndimalakalakatu malangizo anu! Sungani moyo wanga mʼchilungamo chanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ndinalira malangizo anu; Mundipatse moyo mwa cilungamo canu.