Psalms 119:43 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa panga musapaletse mpang'ono pomwe kulankhula mau anu oona, pakuti ndimakhulupirira malangizo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo musandichotsere ndithu mau a choonadi pakamwa panga; pakuti ndinayembekeza maweruzo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musakwatule mawu a choonadi mʼkamwa mwanga, pakuti ndakhazikitsa chiyembekezo changa mʼmalamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo musandicotsere ndithu mau a coonadi pakamwa panga; Pakuti ndinayembekeza maweruzo anu.