Psalms 119:49 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumbukirani mau anu aja kwa ine mtumiki wanu, mau amene amandipatsa chikhulupiriro.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kumbukirani mau a kwa mtumiki wanu, amene munandiyembekezetsa nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumbukirani mawu anu kwa mtumiki wanu, popeza mwandipatsa chiyembekezo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kumbukilani mau a kwa mtumiki wanu, Amene munandiyembekezetsa nao.